05/04/2026
LERO KHRISTU ADAUKA
Lero Khristu anauka,
Ndilo tsiku lokondwera
Iye kale anafera naombola otayika,
Haluluya, haleluya, haleluya, haleluya.
Tiyimbire zomtamira
Ndiye Khristu wa Kumwamba,
Natsikirako kumanda, nalanditsa auipa,
Haluluya, haleluya, haleluya, haleluya
Koma masautso ake anatiombola ife,
Ndiye Mfumu ya mafumu,
Mwana ndithu wa Mulungu.
Haluluya, haleluya, haleluya, haleluya.
Tiyimbire Mlungu wathu, kuti atikonda ndithu,
Mtamenso angelo inu,
Ndiye Tate, Mwana, Mzimu.
Haluluya, haleluya, haleluya, haleluya.
Shared from Chitsitsimutso Mobile App